Genesis 10:22 - Buku Lopatulika22 Ana aamuna a Semu; Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ana amuna a Semu; Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ana a Semu anali Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Onani mutuwo |
Ndipo ndidzaika chizindikiro pakati pao, ndipo ndidzatumiza onse amene apulumuka mwa iwo kwa amitundu, kwa Tarisisi, kwa Puti ndi kwa Aludi, okoka uta kwa Tubala ndi Yavani, kuzisumbu zakutali, amene sanamve mbiri yanga, ngakhale kuona ulemerero wanga; ndipo adzabukitsa ulemerero wanga pakati pa amitundu.