Numeri 24:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo ananena fanizo lake, nati, Ha! Adzakhala ndi moyo ndani pakuchita ichi Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo ananena fanizo lake, nati, Ha! Adzakhala ndi moyo ndani pakuchita ichi Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Adayamba kulankhulanso nati, “Kalanga ine, ndani akhale moyo, Mulungu akachita zimenezi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo ananenanso uthenga wina kuti, “Aa, ndani adzakhala ndi moyo Mulungu akachita zimenezi? Onani mutuwo |