Numeri 24:22 - Buku Lopatulika22 Koma Kaini adzaonongeka, kufikira Asiriya adzakumanga nsinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma Kaini adzaonongeka, kufikira Asiriya adzakumanga nsinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 komabe mudzaonongeka inu ana a Kaini, mudzakhala mu ukapolo wa Asuri nthaŵi yaitali.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 komabe inu Akeni mudzawonongedwa, pamene Asuri adzakutengeni ukapolo.” Onani mutuwo |