Genesis 10:11 - Buku Lopatulika11 M'dziko momwemo iye anatuluka kunka ku Asiriya, namanga Ninive, ndi mzinda wa Rehoboti, ndi Kala, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 M'dziko momwemo iye anatuluka kunka ku Asiriya, namanga Ninive, ndi mudzi wa Rehoboti, ndi Kala, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Iyeyu adachoka ku Sinara nakakhala ku Asiriya, ndipo adakamanga mizinda ya Ninive, Rehobotiiri, Kala, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Atachoka mʼdziko limeneli anapita ku Asiriya kumene anakamanga Ninive, Rehoboti-Iri, Kala, Onani mutuwo |