Genesis 10:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo kuyamba kwake kwa ufumu wake kunali Babiloni, ndi Ereke, ndi Akadi, ndi Kaline, m'dziko la Sinara. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo kuyamba kwake kwa ufumu wake kunali Babiloni, ndi Ereke, ndi Akadi, ndi Kaline, m'dziko la Sinara. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ankalamulira ku Babiloni, ku Ereki, ndi ku Akadi. Maufumu onseŵa anali m'dziko la Sinara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Malo oyambirira a ufumu wake anali Babeli, Ereki, Akadi ndi Kaline. Malo onsewa anali mʼdziko la Sinara. Onani mutuwo |