Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 10:12 - Buku Lopatulika

12 ndi Reseni pakati pa Ninive ndi Kala: umenewo ndi mzinda waukulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 ndi Reseni pakati pa Ninive ndi Kala: umenewo ndi mudzi waukulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 ndi mzinda wa Reseni umene uli pakati pa Ninive ndi mzinda waukulu uja wa Kala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 ndi Reseni, mzinda waukulu umene uli pakati pa Ninive ndi Kala.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:12
3 Mawu Ofanana  

M'dziko momwemo iye anatuluka kunka ku Asiriya, namanga Ninive, ndi mzinda wa Rehoboti, ndi Kala,


Ejipito ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabu, ndi Nafituhimu,


Meseki, Tubala, ndi aunyinji ake onse ali komweko, manda ake amzinga; onsewo osadulidwa, ophedwa ndi lupanga; pakuti anaopsetsa m'dziko la amoyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa