Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 10:13 - Buku Lopatulika

13 Ejipito ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabu, ndi Nafituhimu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ejipito ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabu, ndi Nafituhimu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ejipito ndi amene anali kholo la anthu a ku Ludi, Anamu, Lehabu, Nafutu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:13
5 Mawu Ofanana  

ndi Reseni pakati pa Ninive ndi Kala: umenewo ndi mzinda waukulu.


Ndi ana aamuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani.


Kwerani, inu akavalo; chitani misala, inu magaleta, atuluke amphamvu; Akusi ndi Aputi, ogwira chikopa; ndi Aludi, amene agwira ndi kukoka uta.


Kusi, ndi Puti, ndi Ludi, ndi osokonezeka onse, ndi Libiya, ndi anthu a dziko lopangana nao, adzagwa pamodzi nao ndi lupanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa