Hoseya 14:3 - Buku Lopatulika3 Asiriya sadzatipulumutsa; sitidzayenda pa akavalo, ndipo sitidzanenanso kwa ntchito ya manja athu, Inu ndinu milungu yathu; pakuti mwa Inu ana amasiye apeza chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Asiriya sadzatipulumutsa; sitidzayenda pa akavalo, ndipo sitidzanenanso kwa ntchito ya manja athu, Inu ndinu milungu yathu; pakuti mwa Inu ana amasiye apeza chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Aasiriya sadzatipulumutsa, akavalo ankhondo sadzatiteteza. Chimene tidapanga ndi manja athu sitidzachitchulanso kuti, ‘Mulungu wathu,’ pakuti ndinu amene mumachitira chifundo amasiye.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Asiriya sangatipulumutse; ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo, sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’ kwa zimene manja athu omwe anazipanga, pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.” Onani mutuwo |