Hoseya 14:2 - Buku Lopatulika2 Mukani nao mau, nimubwerere kwa Yehova; nenani kwa Iye, Chotsani mphulupulu zonse, nimulandire chokoma; ndipo tidzapereka mau milomo yathu ngati ng'ombe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mukani nao mau, nimubwerere kwa Yehova; nenani kwa Iye, Chotsani mphulupulu zonse, nimulandire chokoma; ndipo tidzapereka mau milomo yathu ngati ng'ombe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Bwererani kwa Chauta, ndipo mumpemphe kuti, “Mutikhululukire machimo athu onse. Mumvere pempho lathu ndipo tidzakuyamikani ndi mau otamanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Bweretsani zopempha zanu ndipo bwererani kwa Yehova. Munene kwa Iye kuti, “Tikhululukireni machimo athu onse ndi kutilandira mokoma mtima, kuti tithe kukuyamikani ndi mawu a pakamwa pathu. Onani mutuwo |