Hoseya 14:1 - Buku Lopatulika1 Israele, bwerera kunka kwa Yehova Mulungu wako; pakuti wagwa mwa mphulupulu yako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Israele, bwerera kunka kwa Yehova Mulungu wako; pakuti wagwa mwa mphulupulu yako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Aisraele, bwererani kwa Chauta, Mulungu wanu, pakuti mwagwa chifukwa cha machimo anu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako. Machimo anu ndi amene akugwetsani! Onani mutuwo |