Hoseya 14:4 - Buku Lopatulika4 Ndidzachiritsa kubwerera kwao, ndidzawakonda mwaufulu; pakuti mkwiyo wanga wamchokera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndidzachiritsa kubwerera kwao, ndidzawakonda mwaufulu; pakuti mkwiyo wanga wamchokera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta akuti, “Ndidzachiza matenda ao a kusakhulupirika. Ndidzaŵakonda kwambiri, pakuti ndaleka kuŵakwiyira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo ndipo ndidzawakonda mwaufulu pakuti ndaleka kuwakwiyira. Onani mutuwo |