Hoseya 14:5 - Buku Lopatulika5 Ndidzakhala kwa Israele ngati mame; adzachita maluwa ngati kakombo, ndi kutambalalitsa mizu yake ngati Lebanoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndidzakhala kwa Israele ngati mame; adzachita maluwa ngati kakombo, ndi kutambalalitsa mizu yake ngati Lebanoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndidzatsitsimutsa Israele ngati mame. Adzachita maluŵa ngati kakombo, adzazika mizu ngati mtengo wa ku Lebanoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli Ndipo iye adzachita maluwa ngati kakombo. Adzazika mizu yake pansi ngati mkungudza wa ku Lebanoni; Onani mutuwo |