Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:4 - Buku Lopatulika

nakhala upo wakuti amgwire Yesu ndi chinyengo, namuphe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nakhala upo wakuti amgwire Yesu ndi chinyengo, namuphe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ankakambirana za njira yoti agwirire Yesu mochenjera, nkumupha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo anapangana kuti amugwire Yesu mobisa ndi kumupha.

Onani mutuwo



Mateyu 26:4
10 Mawu Ofanana  

Ndipo njoka inali yochenjera yoposa zamoyo zonse za m'thengo zimene anazipanga Yehova Mulungu. Ndipo inati kwa mkaziyo, Eya! Kodi anatitu Mulungu, Usadye mitengo yonse ya m'mundamu?


Adzikhazikitsa mafumu a dziko lapansi, nachita upo akulu pamodzi, Kutsutsana naye Yehova, ndi Wodzozedwa wake, ndi kuti,


Usabisalire, woipa iwe, pomanga wolungama; usapasule popuma iyepo.


Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga.


Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthawa kulanga kwake kwa Gehena?


Ndipo popita masiku awiri kuli phwando la Paska ndi Mkate wopanda chotupitsa; ndipo ansembe aakulu ndi alembi anafunafuna momchitira chiwembu, ndi kumupha:


Chifukwa chake, kuyambira tsiku lomwelo anapangana kuti amuphe Iye.


nati, Wodzala ndi chinyengo chonse ndi chenjerero lonse, iwe, mwana wa mdierekezi, mdani wa chilungamo chonse, kodi sudzaleka kuipsa njira zolunjika za Ambuye?


Imeneyo inachenjerera fuko lathu, niwachitira choipa makolo athu, niwatayitsa tiana tao, kuti tingakhale ndi moyo.


Koma ndiopa, kuti pena, monga njoka inanyenga Heva ndi kuchenjerera kwake, maganizo anu angaipsidwe kusiyana nako kuona mtima ndi kuyera mtima zili kwa Khristu.