Yohane 11:53 - Buku Lopatulika53 Chifukwa chake, kuyambira tsiku lomwelo anapangana kuti amuphe Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Chifukwa chake, kuyambira tsiku lomwelo anapangana kuti amuphe Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Kuyambira tsiku limenelo akulu aja a Ayuda adayamba kupangana zoti amuphe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Choncho kuyambira tsiku limeneli iwo anakonzekera za kuti amuphe. Onani mutuwo |