Yohane 11:52 - Buku Lopatulika52 ndipo si chifukwa cha mtunduwo wokha ai, koma kuti akasonkhanitse pamodzi ana a Mulungu akubalalikawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 ndipo si chifukwa cha mtunduwo wokha ai, koma kuti akasonkhanitse pamodzi ana a Mulungu akubalalikawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Tsono osati kungofera fuko chabe, komanso kusonkhanitsa pamodzi ana a Mulungu amene adabalalika.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 ndipo osati mtundu okhawo komanso kwa ana ena a Mulungu onse obalalikana, kuti awabweretse pamodzi ndi kuwapanga kukhala amodzi. Onani mutuwo |