Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:19 - Buku Lopatulika

19 Imeneyo inachenjerera fuko lathu, niwachitira choipa makolo athu, niwatayitsa tiana tao, kuti tingakhale ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Imeneyo inachenjerera fuko lathu, niwachitira choipa makolo athu, niwatayitsa tiana tao, kuti tingakhale ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Mfumuyo idachenjerera mtundu wathu, nkuyamba kuzunza makolo athu, pakuŵatayitsa ana ao akhanda kuti asakhale ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mfumuyo inachita mwachinyengo ndi mtundu wathu ndi kuwazunza kuti ataye ana awo akhanda kuti afe.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:19
6 Mawu Ofanana  

Anasanduliza mitima yao, kuti adane nao anthu ake, kuti achite monyenga ndi atumiki ake.


Pamenepo inalowa mfumu yatsopano mu ufumu wa Ejipito, imene siinadziwe Yosefe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa