Mateyu 12:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pamenepo Afarisi aja adatuluka nakachita upo kuti apangane njira yophera Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma Afarisi anatuluka kunja ndi kukonza njira yoti amuphere. Onani mutuwo |