Mateyu 26:5 - Buku Lopatulika5 Koma ananena iwo, pa nthawi ya chikondwerero iai, kuti pasakhale phokoso la anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma ananena iwo, pa nthawi la chikondwerero iai, kuti pasakhale phokoso la anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma ankati, “Zimenezi tisadzachite pa nthaŵi ya chikondwerero ai, pangadzachitike chipolowe pakati pa anthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo anati, “Osati nthawi yaphwando chifukwa pangabuke chipolowe pakati pa anthu.” Onani mutuwo |