Mateyu 26:4 - Buku Lopatulika4 nakhala upo wakuti amgwire Yesu ndi chinyengo, namuphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 nakhala upo wakuti amgwire Yesu ndi chinyengo, namuphe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ankakambirana za njira yoti agwirire Yesu mochenjera, nkumupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 ndipo anapangana kuti amugwire Yesu mobisa ndi kumupha. Onani mutuwo |