Mateyu 23:33 - Buku Lopatulika33 Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthawa kulanga kwake kwa Gehena? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthawa kulanga kwake kwa Gehena? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 “Njoka inu, ana a mamba, mudzachipeŵa bwanji chilango cha ku Gehena? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 “Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? Onani mutuwo |