Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 9:3 - Buku Lopatulika

Pobwerera m'mbuyo adani anga, akhumudwa naonongeka pankhope panu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pobwerera m'mbuyo adani anga, akhumudwa naonongeka pankhope panu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mukangofika, adani anga amathaŵa, amaphunthwa ndi kufa pamaso panu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Adani anga amathawa, iwo amapunthwa ndi kuwonongedwa pamaso panu.

Onani mutuwo



Masalimo 9:3
9 Mawu Ofanana  

Inu ndinu woopsa; ndipo utauka mkwiyo wanu adzakhala chilili ndani pamaso panu?


Unapserera ndi moto, unadulidwa; aonongeka pa kudzudzula kwa nkhope yanu.


Popeza udati, Inu Yehova, ndinu pothawirapo panga! Udaika Wam'mwambamwamba chokhalamo chako;


Kuonetsera chifundo chanu mamawa, ndi chikhulupiriko chanu usiku uliwonse.


Pamene Inu munachita zinthu zoopsa, zimene ife sitinayang'anira, Inu munatsika, mapiri anagwedezeka pamaso panu.


amene adzamva chilango, ndicho chionongeko chosatha chowasiyanitsa kunkhope ya Ambuye, ndi kuulemerero wa mphamvu yake,


Ndipo ndinaona, mpando wachifumu waukulu woyera, ndi Iye wakukhalapo, amene dziko ndi m'mwamba zinathawa pamaso pake, ndipo sanapezedwe malo ao.