Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 91:9 - Buku Lopatulika

9 Popeza udati, Inu Yehova, ndinu pothawirapo panga! Udaika Wam'mwambamwamba chokhalamo chako;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Popeza udati, Inu Yehova, ndinu pothawirapo panga! Udaika Wam'mwambamwamba chokhalamo chako;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Chifukwa chakuti wavomera Chauta kuti akhale malo ako othaŵirako, wavomera Wopambanazonse kuti akhale malo ako okhalamo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo; wavomera Yehova kukhala kothawira kwako.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 91:9
6 Mawu Ofanana  

Mundikhalire thanthwe lokhalamo, lopitako kosaleka; mwalamulira kundipulumutsa; popeza Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa.


Pobwerera m'mbuyo adani anga, akhumudwa naonongeka pankhope panu.


Ambuye, Inu munatikhalira mokhalamo m'mibadwomibadwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa