Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 91:10 - Buku Lopatulika

10 palibe choipa chidzakugwera, ndipo cholanga sichidzayandikiza hema wako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 palibe choipa chidzakugwera, ndipo cholanga sichidzayandikiza hema wako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 zoipa sizidzakugwera, zoopsa sizidzafika pafupi ndi nyumba yako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Choncho palibe choyipa chimene chidzakugwera, zoopsa sizidzafika pafupi ndi tenti yako.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 91:10
5 Mawu Ofanana  

Ndipo udzapeza kuti pahema pako mpa mtendere; nudzazonda za m'banja mwako osasowapo kanthu.


Yehova adzakusunga kukuchotsera zoipa zilizonse; adzasunga moyo wako.


Palibe vuto lidzagwera wolungama; koma amphulupulu adzadzazidwa ndi zoipa.


Koma ngati tiyembekezera chimene sitichipenya, pomwepo tichilindirira ndi chipiriro.


Ndipo Yehova adzakuchotserani nthenda zonse; sadzakuikirani nthenda zoipa zilizonse za Aejipito muzidziwa zija; koma adzaziika pa onse akudana ndi inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa