Masalimo 91:8 - Buku Lopatulika8 Koma udzapenya ndi maso ako, nudzaona kubwezera chilango oipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma udzapenya ndi maso ako, nudzaona kubwezera chilango oipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Uzingopenya ndi maso ako, ndipo udzaona m'mene amalangidwira anthu ochita zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Udzapenya ndi maso ako ndipo udzaona mmene anthu oyipa amalangidwira. Onani mutuwo |