Masalimo 80:16 - Buku Lopatulika16 Unapserera ndi moto, unadulidwa; aonongeka pa kudzudzula kwa nkhope yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Unapserera ndi moto, unadulidwa; aonongeka pa kudzudzula kwa nkhope yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Adani athu autentha, augwetsa pansi. Ayang'aneni iwowo mokwiya ndi kuŵaononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Mpesa wanu wadulidwa ndi kutenthedwa ndi moto; pakudzudzula kwanu anthu anu awonongeka. Onani mutuwo |