Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 80:15 - Buku Lopatulika

15 ndi tsinde limene dzanja lanu lamanja linaoka, ndi mphanda munadzilimbikitsira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndi tsinde limene dzanja lanu lamanja linaoka, ndi mphanda munadzilimbikitsira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 mtengo woyambirira umene Inu mudaubzala ndi dzanja lanu lamanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala, mwana amene inu munamukuza nokha.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:15
16 Mawu Ofanana  

Mudatenga mpesa kuchokera ku Ejipito, munapirikitsa amitundu ndi kuuoka uwu.


Amene dzanja langa lidzakhazikika naye; inde mkono wanga udzalimbitsa.


Bwerani, Yehova; kufikira liti? Ndipo alekeni atumiki anu.


Ndipo padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese, ndi nthambi yotuluka m'mizu yake idzabala zipatso;


Ndipo tsopano, ati Yehova, amene anandiumba Ine ndisanabadwe ndikhale mtumiki wake, kubwezanso Yakobo kwa Iye, ndi kuti Israele asonkhanidwe kwa Iye; chifukwa Ine ndili wolemekezeka pamaso pa Yehova, ndipo Mulungu wanga wakhala mphamvu zanga;


Tayang'anani kunsi kuchokera kumwamba, taonani pokhala panu poyera, ndi pa ulemerero wanu, changu chanu ndi ntchito zanu zamphamvu zili kuti? Mwanditsekerezera zofunafuna za mtima wanu ndi chisoni chanu.


Ndipo Ine ndinakuoka mpesa wangwiro, mbeu yoona; kodi bwanji wandisandukira Ine mbeu yopanda pake, ya mpesa wachilendo?


kufikira Yehova adzazolika kumwamba ndi kuona.


Tamvera tsono, Yoswa mkulu wa ansembe, iwe ndi anzako akukhala pansi pamaso pako; pakuti iwo ndiwo chizindikiro; pakuti taonani, ndidzafikitsa mtumiki wanga, ndiye Mphukira.


nunene naye, kuti, Atero Yehova wa makamu, ndi kuti, Taonani, munthu dzina lake ndilo Mphukira, ndipo adzaphuka m'malo mwake, nadzamanga Kachisi wa Yehova:


Ndipo Iye anayamba kulankhula nao m'mafanizo. Munthu analima munda wampesa, nauzunguniza ndi linga, nakumba moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina.


Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate wanga ndiye wam'munda.


Penyani muli mokhalamo mwanu mopatulika, m'mwamba, ndipo dalitsani anthu anu Israele, ndi nthaka imene munatipatsa, monga munalumbirira makolo athu, dziko moyenda mkaka ndi uchi ngati madzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa