Masalimo 80:17 - Buku Lopatulika17 Dzanja lanu likhale pa munthu wa padzanja lamanja lanu; pa mwana wa munthu amene munadzilimbikitsira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Dzanja lanu likhale pa munthu wa pa dzanja lamanja lanu; pa mwana wa munthu amene munadzilimbikitsira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma ndi dzanja lanu muteteze anthu amene mudaŵasankha, anthu amene Inu nomwe mwaŵalimbikitsa kuti akutumikireni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Dzanja lanu likhale pa munthu amene ali ku dzanja lanu lamanja, mwana wa munthu amene mwalera nokha. Onani mutuwo |