Masalimo 9:2 - Buku Lopatulika2 Ndidzakondwerera ndi kusekera mwa Inu; ndidzaimbira dzina lanu, Wam'mwambamwamba Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidzakondwerera ndi kusekera mwa Inu; ndidzaimbira dzina lanu, Wam'mwambamwamba Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndidzakondwa ndi kusangalala chifukwa cha Inu, ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu, Inu Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzakondwa ndi kusangalala mwa inu; Ndidzayimba nyimbo zamatamando pa dzina lanu, Inu Wammwambamwamba. Onani mutuwo |