Masalimo 92:2 - Buku Lopatulika2 Kuonetsera chifundo chanu mamawa, ndi chikhulupiriko chanu usiku uliwonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kuonetsera chifundo chanu mamawa, ndi chikhulupiriko chanu usiku uliwonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nkwabwino m'maŵa kulalika za chikondi chanu chosasinthika, ndipo usiku kusimba za kukhulupirika kwanu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kulengeza chikondi chanu mmawa, ndi kukhulupirika kwanu nthawi ya usiku, Onani mutuwo |