Masalimo 92:3 - Buku Lopatulika3 Pa choimbira cha zingwe khumi ndi pachisakasa; pazeze ndi kulira kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pa choimbira cha zingwe khumi ndi pachisakasa; pazeze ndi kulira kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 poimba nyimbo zokoma ndi gitara, zeze ndi pangwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi ndi mayimbidwe abwino a zeze. Onani mutuwo |