Masalimo 92:4 - Buku Lopatulika4 Popeza Inu, Yehova, munandikondweretsa ndi kuchita kwanu, ndidzafuula mokondwera pa ntchito ya manja anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Popeza Inu, Yehova, munandikondweretsa ndi kuchita kwanu, ndidzafuula mokondwera pa ntchito ya manja anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Inu Chauta, mwandisangalatsa ndi ntchito zanu. Motero ndikufuula ndi chimwemwe chifukwa cha zimene Inu mwachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti Inu mumandisangalatsa ndi ntchito zanu, Inu Yehova; Ine ndikuyimba mwachimwemwe pa ntchito ya manja anu. Onani mutuwo |