Masalimo 92:5 - Buku Lopatulika5 Ha! Ntchito zanu nzazikulu, Yehova, zolingalira zanu nzozama ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ha! Ntchito zanu nzazikulu, Yehova, zolingalira zanu nzozama ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ntchito zanu si kukula kwake, Inu Chauta! Maganizo anu si kuzama kwake! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndi yayikuludi ntchito yanu Yehova, maganizo anu ndi ozamadi! Onani mutuwo |