Masalimo 92:1 - Buku Lopatulika1 Nkokoma kuyamika Yehova, ndi kuimbira nyimbo dzina lanu, Wam'mwambamwamba Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Nkokoma kuyamika Yehova, ndi kuimbira nyimbo dzina lanu, Wam'mwambamwamba Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nkwabwino kuthokoza Chauta, kuimba nyimbo zotamanda dzina lanu, Inu Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nʼkwabwino kutamanda Yehova ndi kuyimbira nyimbo dzina lanu, Inu Wammwambamwamba, Onani mutuwo |