Masalimo 91:16 - Buku Lopatulika16 Ndidzamkhutitsa ndi masiku ambiri, ndi kumuonetsera chipulumutso changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndidzamkhutitsa ndi masiku ambiri, ndi kumuonetsera chipulumutso changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndidzampatsa moyo wautali ndi kumpulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndidzamupatsa moyo wautali ndi kumupulumutsa.” Onani mutuwo |