Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 91:16 - Buku Lopatulika

16 Ndidzamkhutitsa ndi masiku ambiri, ndi kumuonetsera chipulumutso changa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndidzamkhutitsa ndi masiku ambiri, ndi kumuonetsera chipulumutso changa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ndidzampatsa moyo wautali ndi kumpulumutsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ndidzamupatsa moyo wautali ndi kumupulumutsa.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 91:16
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamwalira, nafa mu ukalamba wake wabwino, nkhalamba ya zaka zambiri; natengedwa akhale ndi a mtundu wake.


Udzafika kumanda utakalamba, monga abwera nao mtolo wa tirigu m'nyengo yake.


Mudzandidziwitsa njira ya moyo, pankhope panu pali chimwemwe chokwanira; m'dzanja lanu lamanja muli zokondweretsa zomka muyaya.


Anakupemphani moyo, mwampatsa iye; mwamtalikitsira masiku kunthawi za nthawi.


Wopereka nsembe yachiyamiko andilemekeza Ine; ndipo kwa iye wosunga mayendedwe ake ndidzamuonetsa chipulumutso cha Mulungu.


Kuopa Yehova kutanimphitsa masiku; koma zaka za oipa zidzafinimpha.


Mphotho ya chifatso ndi kuopa Yehova ndiye chuma, ndi ulemu, ndi moyo.


Masiku ambiri ali m'dzanja lamanja lake; chuma ndi ulemu m'dzanja lake lamanzere.


pakuti adzakuonjezera masiku ambiri, ndi zaka za moyo ndi mtendere.


Koma Israele adzapulumutsidwa ndi Yehova ndi chipulumutso chosatha; inu simudzakhala ndi manyazi, pena kuthedwa nzeru kunthawi zosatha.


chifukwa maso anga adaona chipulumutso chanu,


ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.


kuti muope Yehova Mulungu wanu, kusunga malemba ake onse ndi malamulo ake, amene ndikuuzani inu ndi ana anu, ndi zidzukulu zanu, masiku onse a moyo wanu, ndi kuti masiku anu achuluke.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa