Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 83:6 - Buku Lopatulika

Mahema a Edomu ndi a Aismaele; Mowabu ndi Ahagiri;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mahema a Edomu ndi a Aismaele; Mowabu ndi Ahagiri;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

anthu okhala m'mahema a Aedomu ndi Aismaele, Amowabu ndi Ahagara,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Matenti a Edomu ndi Aismaeli, Mowabu ndi Ahagiri,

Onani mutuwo



Masalimo 83:6
9 Mawu Ofanana  

Ndipo masiku a Saulo anagwirana nkhondo ndi Ahagiri, amene adagwa ndi dzanja lao; ndipo anakhala m'mahema mwao kum'mawa konse kwa Giliyadi.


Ndipo zitatha izi, kunachitika kuti ana a Mowabu, ndi ana a Amoni, ndi ena pamodzi ndi Aamoni, anadza kuyambana nkhondo ndi Yehosafati.


Yehova, kumbukirani ana a Edomu tsiku la Yerusalemu; amene adati, Gamulani, gamulani, kufikira maziko ake.


Adzikhazikitsa mafumu a dziko lapansi, nachita upo akulu pamodzi, Kutsutsana naye Yehova, ndi Wodzozedwa wake, ndi kuti,


Ndipo Mowabu adzaonongeka asakhalenso mtundu wa anthu, chifukwa anadzikuzira yekha pa Yehova.


Ndipo anadzisonkhanitsira ana a Amoni ndi a Amaleke, namuka nakantha Israele, nalanda mzinda wa m'migwalangwa nakhalamo.