Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 5:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo masiku a Saulo anagwirana nkhondo ndi Ahagiri, amene adagwa ndi dzanja lao; ndipo anakhala m'mahema mwao kum'mawa konse kwa Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo masiku a Saulo anagwirana nkhondo ndi Ahagiri, amene adagwa ndi dzanja lao; ndipo anakhala m'mahema mwao kum'mawa konse kwa Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pa nthaŵi ya Saulo, Arubeni adathira nkhondo Ahagiri ndi kuŵagonjetsa, kenaka adakhala m'mahema mwao m'dziko lonselo kuvuma kwa Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Pa nthawi ya Sauli anachita nkhondo ndi Ahagiri ndi kuwagonjetsa. Tsono iwo anakhala mʼmatenti a Ahagiri ku dera lonse la kummawa kwa Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 5:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Sara anaona mwana wake wamwamuna wa Hagara Mwejipito, amene anambalira Abrahamu, alinkuseka.


Mibadwo ya Ismaele mwana wamwamuna wa Abrahamu, amene Hagara Mwejipito mdzakazi wa Sara anambalira Abrahamu ndi iyi:


ndi woyang'anira zoweta zazing'ono ndiye Yazizi Mhagiri. Onsewa ndiwo akulu a zolemera zake za mfumu Davide.


Mahema a Edomu ndi a Aismaele; Mowabu ndi Ahagiri;


Gebala ndi Amoni ndi Amaleke; Filistiya, pamodzi ndi iwo okhala mu Tiro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa