2 Mbiri 20:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo zitatha izi, kunachitika kuti ana a Mowabu, ndi ana a Amoni, ndi ena pamodzi ndi Aamoni, anadza kuyambana nkhondo ndi Yehosafati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo zitatha izi, kunachitika kuti ana a Mowabu, ndi ana a Amoni, ndi ena pamodzi ndi Aamoni, anadza kuyambana nkhondo ndi Yehosafati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nthaŵi ina, Amowabu, Aamoni ndi Ameuni ena adabwera kudzamenyana nkhondo ndi Yehosafati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Zitatha izi, Amowabu ndi Aamoni pamodzi ndi Ameuni ena anabwera kudzachita nkhondo ndi Yehosafati. Onani mutuwo |