Masalimo 83:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti anakhalira upo ndi mtima umodzi; anachita chipangano cha pa Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti anakhalira upo ndi mtima umodzi; anachita chipangano cha pa Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Zoonadi, akumvana popangana chiwembu, akupangana zokuukirani, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu; Iwo achita mgwirizano kutsutsana nanu: Onani mutuwo |