Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 70:1 - Buku Lopatulika

Fulumirani kundipulumutsa, Mulungu! Fulumirani kundithandiza, Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Fulumirani kundipulumutsa, Mulungu! Fulumirani kundithandiza, Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, pulumutseni. Inu Chauta, fulumirani kudzandithandiza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.

Onani mutuwo



Masalimo 70:1
6 Mawu Ofanana  

Fulumirani ndiyankheni, Yehova; mzimu wanga ukutha. Musandibisire nkhope yanu; ndingafanane nao akutsikira kudzenje.


Yehova, musandidzudzule ndi mkwiyo wanu, ndipo musandilange moopsa m'mtima mwanu.


Yandikizani moyo wanga, ndi kuuombola; ndipulumutseni chifukwa cha adani anga.


Musandikhalire kutali, Mulungu; fulumirani kundithandiza, Mulungu.