Masalimo 69:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo mbumba ya atumiki ake idzalilandira; ndipo iwo akukonda dzina lake adzakhala m'mwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo mbumba ya atumiki ake idzalilandira; ndipo iwo akukonda dzina lake adzakhala m'mwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Ana a atumiki ake nawonso adzalilandira kuti likhale lao, ndipo okonda Mulungu adzakhala m'menemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 ana atumiki ake adzalitenga kukhala cholowa chawo, ndipo iwo amene amakonda dzina lake adzakhala kumeneko. Onani mutuwo |