Masalimo 69:35 - Buku Lopatulika35 Pakuti Mulungu adzapulumutsa Ziyoni, nadzamanga mizinda ya Yuda; ndipo iwo adzakhala komweko, likhale laolao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Pakuti Mulungu adzapulumutsa Ziyoni, nadzamanga midzi ya Yuda; ndipo iwo adzakhala komweko, likhale laolao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Mulungu adzapulumutsa Ziyoni, ndipo adzamanganso mizinda ya Yuda. Anthu ake adzakhala kumeneko, ndipo lidzakhala dziko lao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 pakuti Mulungu adzapulumutsa Ziyoni ndi kumanganso mizinda ya Yuda, anthu adzakhala kumeneko ndipo dzikolo lidzakhala lawo; Onani mutuwo |