Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:34 - Buku Lopatulika

Zakumwamba ndi dziko lapansi zimlemekeze, nyanja ndi zonse zoyenda m'mwemo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zakumwamba ndi dziko lapansi zimlemekeze, nyanja ndi zonse zoyenda m'mwemo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kumwamba ndi pansi pano, nyanja ndi zonse zoyenda m'menemo zitamande Iye.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kumwamba ndi dziko lapansi zitamanda Iye, nyanja ndi zonse zomwe zimayenda mʼmenemo,

Onani mutuwo



Masalimo 69:34
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anati Mulungu, Madzi abale zochuluka zamoyo zoyendayenda, ndi mbalame ziuluke pamwamba padziko lapansi ndi pamlengalenga.


Ichi adzachilembera mbadwo ukudza; ndi mtundu wa anthu umene udalengedwa udzamlemekeza Yehova.


Zonse zakupuma zilemekeze Yehova. Aleluya.


Kumwamba kukondwere nilisekerere dziko lapansi; nyanja ibume mwa kudzala kwake.


Imbani inu, m'mwamba, nukondwere iwe dziko lapansi, imbani inu mapiri, pakuti Yehova watonthoza mtima wa anthu ake, nadzachitira chifundo ovutidwa ake.


Pakuti inu mudzatuluka ndi kukondwa, ndi kutsogozedwa ndi mtendere; mapiri ndi zitunda, zidzaimba zolimba pamaso panu, ndi mitengo yonse ya m'thengo idzaomba m'manja mwao.