Masalimo 102:18 - Buku Lopatulika18 Ichi adzachilembera mbadwo ukudza; ndi mtundu wa anthu umene udalengedwa udzamlemekeza Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ichi adzachilembera mbadwo ukudza; ndi mtundu wa anthu umene udalengedwa udzamlemekeza Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Zimenezi zilembedwe chifukwa cha mbadwo wakutsogolo, kuti anthu amene mpaka tsopano lino sanabadwebe, nawonso adzatamande Chauta, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Zimenezi zilembedwe chifukwa cha mibado ya mʼtsogolo, kuti anthu amene sanabadwe adzatamande Yehova: Onani mutuwo |