Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 2:3 - Buku Lopatulika

Tidule zomangira zao, titaye nsinga zao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tidule zomangira zao, titaye nsinga zao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akuti, “Tiyeni timasule maunyolo aoŵa, tichokeretu mu ulamuliro wao.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”

Onani mutuwo



Masalimo 2:3
5 Mawu Ofanana  

Pakuti kale lomwe ndinathyola goli lako, ndi kudula zomangira zako; ndipo unati, Sindidzakutumikirani, pakuti pa zitunda zonse zazitali, ndi patsinde pa mitengo yonse yaiwisi unawerama, ndi kuchita dama.


Ine ndidzanka kwa akulu, ndidzanena ndi iwo; pakuti adziwa njira ya Yehova, ndi chiweruzo cha Mulungu wao. Koma awa anavomerezana nathyola goli, nadula zomangira zao.


Koma mfulu za pamudzi pake zinamuda, nkutuma akazembe amtsate m'mbuyo ndi kunena, Ife sitifuna munthuyo akhale mfumu yathu.


Koma adani anga aja osafuna kuti ndidzakhala mfumu yao, bwerani nao kuno, nimuwaphe pamaso panga.