Masalimo 2:4 - Buku Lopatulika4 Wokhala m'mwambayo adzaseka; Ambuye adzawanyoza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Wokhala m'mwambayo adzaseka; Ambuye adzawanyoza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta amene amalamulira kumwambako akungoŵaseka ndi kuŵanyoza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo. Onani mutuwo |