Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 2:3 - Buku Lopatulika

3 Tidule zomangira zao, titaye nsinga zao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Tidule zomangira zao, titaye nsinga zao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Akuti, “Tiyeni timasule maunyolo aoŵa, tichokeretu mu ulamuliro wao.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 2:3
5 Mawu Ofanana  

Pakuti kale lomwe ndinathyola goli lako, ndi kudula zomangira zako; ndipo unati, Sindidzakutumikirani, pakuti pa zitunda zonse zazitali, ndi patsinde pa mitengo yonse yaiwisi unawerama, ndi kuchita dama.


Ine ndidzanka kwa akulu, ndidzanena ndi iwo; pakuti adziwa njira ya Yehova, ndi chiweruzo cha Mulungu wao. Koma awa anavomerezana nathyola goli, nadula zomangira zao.


Koma mfulu za pamudzi pake zinamuda, nkutuma akazembe amtsate m'mbuyo ndi kunena, Ife sitifuna munthuyo akhale mfumu yathu.


Koma adani anga aja osafuna kuti ndidzakhala mfumu yao, bwerani nao kuno, nimuwaphe pamaso panga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa