Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 2:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Tidule zomangira zao, titaye nsinga zao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Tidule zomangira zao, titaye nsinga zao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Akuti, “Tiyeni timasule maunyolo aoŵa, tichokeretu mu ulamuliro wao.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 2:3
5 Mawu Ofanana  

“Kuyambira kalekale inu munathyola goli lanu ndi kudula msinga zanu; munanena kuti, ‘Sitidzakutumikirani!’ Ndithudi, inu mwakhala ngati mkazi wachiwerewere. Mukupembedza milungu ina pa phiri lililonse lalitali ndiponso pansi pa mtengo uliwonse wa masamba ambiri.


Tsono ndidzapita kwa atsogoleri ndi kukayankhula nawo; ndithu iwo amadziwa njira ya Yehova, amadziwa zomwe Mulungu wawo amafuna.” Koma ayi, iwonso anathyola goli la Yehova ndipo anadula msinga zawo.


“Koma anthu ake anamuda ndipo anatuma nthumwi pambuyo pake kukanena kuti, ‘Sitikufuna munthuyu kuti akhale mfumu yathu.’


Tsono adani anga aja amene sankafuna kuti ndikhale mfumu yawo, abweretseni pano ndi kuwapha ine ndikuona.”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa