Yeremiya 5:5 - Buku Lopatulika5 Ine ndidzanka kwa akulu, ndidzanena ndi iwo; pakuti adziwa njira ya Yehova, ndi chiweruzo cha Mulungu wao. Koma awa anavomerezana nathyola goli, nadula zomangira zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ine ndidzanka kwa akulu, ndidzanena ndi iwo; pakuti adziwa njira ya Yehova, ndi chiweruzo cha Mulungu wao. Koma awa anavomerezana nathyola goli, nadula zomangira zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono ndidzapita kwa akuluakulu, ndidzalankhula ndi amenewo. Pakuti ndiwo angadziŵe njira ya Chauta, ndi zimene Mulungu wao akufuna.” Koma ndidaona kuti iwowonso adathyola goli la Chauta, adadula nsinga zao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsono ndidzapita kwa atsogoleri ndi kukayankhula nawo; ndithu iwo amadziwa njira ya Yehova, amadziwa zomwe Mulungu wawo amafuna.” Koma ayi, iwonso anathyola goli la Yehova ndipo anadula msinga zawo. Onani mutuwo |