Yeremiya 5:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ine ndinati, Ndithu amenewo ali aumphawi; ali opusa; pakuti sadziwa njira ya Yehova, kapena chiweruzo cha Mulungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ine ndinati, Ndithu amenewo ali aumphawi; ali opusa; pakuti sadziwa njira ya Yehova, kapena chiweruzo cha Mulungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Apo ndidati, “Ndi amphaŵi chabe aŵa, alibe ndi nzeru zomwe. Iwo sadziŵa njira ya Chauta, sazindikira zimene Mulungu wao akufuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndiye ndinati, “Awa ndi amphawi chabe; anthu ochita zopusa. Sadziwa njira ya Yehova, sazindikira zimene Mulungu wawo amafuna. Onani mutuwo |