Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 148:5 - Buku Lopatulika

Alemekeze dzina la Yehova; popeza analamulira, ndipo zinalengedwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Alemekeze dzina la Yehova; popeza analamulira, ndipo zinalengedwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zonsezo zitamande dzina la Chauta! Paja Iye adaalamula, izo nkulengedwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zonse zitamande dzina la Yehova pakuti Iye analamula ndipo zinalengedwa.

Onani mutuwo



Masalimo 148:5
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anati Mulungu, Pakhale thambo pakati pamadzi, lilekanitse madzi ndi madzi.


Lemekezani Yehova, inu angelo ake; a mphamvu zolimba, akuchita mau ake, akumvera liu la mau ake.


Nyanja ndi yake, anailenga; ndipo manja ake anaumba dziko louma.


ndiye amene amanga zipinda zake zosanja m'mwamba, nakhazika tsindwi lake padziko lapansi; Iye amene aitana madzi a m'nyanja, nawatsanulira padziko; dzina lake ndiye Yehova.


Muyenera inu, Ambuye wathu, ndi Mulungu wathu, kulandira ulemerero ndi ulemu ndi mphamvu; chifukwa mudalenga zonse, ndipo mwa chifuniro chanu zinakhala, ndipo zinalengedwa.